spot_imgspot_img
Sunday, March 23, 2025
spot_img
spot_img
HomeLatestAmangidwa kamba kothira "batire" ng'ombe mpaka kuipatsa mimba

Amangidwa kamba kothira “batire” ng’ombe mpaka kuipatsa mimba

Apolisi m’boma la Chitipa amanga mkulu wina pomuganizira kuti amachita zachisembwere ndi ng’ombe.

Malingana ndi ofalitsankhani za apolisi ku Chitipa, a Gladwell Simwaka, anthu ena adamupezelera mkuluyo, yemwe ndi James Mtambo wazaka 25, usiku wapa 21 akuchita zadamazo ndi ng’ombe.

Mkuluyo akuyembekezeka kuzengedwa mlandu ogona ndi chiweto, zomwe ndizosephana ndi malamulo adziko lino.

RELATED ARTICLES

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

- Advertisment -

Most Popular