spot_imgspot_img
Tuesday, March 25, 2025
spot_img
spot_img
HomeLatestDPP ikhala kotsutsa kwa zaka 60-Chimwendo Banda

DPP ikhala kotsutsa kwa zaka 60-Chimwendo Banda

Mtsogoleli wa zokambirana ku nyumba ya malamulo Richard Chimwendo Banda wati chipani chotsutsa cha DPP chikhala mbaliyi kwa 60 zikudzazi.

Chimwendo Banda wati mtsogoleri wa dziko lino Dr. Lazarus Chakwera sakuchoka m’boma potengera kuti wapanga chitukuko mosakondera dera lililonse.

Iwo ati boma la DPP linawononga zinthu zambiri m’dziko muno ndipo nkosatheka kuti litengeso boma pa zisankho za chaka chino.

Chimwendo Banda wanena izi mnyumba ya malamulo.

RELATED ARTICLES

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

- Advertisment -

Most Popular