spot_imgspot_img
Monday, April 14, 2025
spot_img
spot_img
HomeLatestKulowa m'boma kwa Chipani cha MCP ndi ngozi yomwe simayenera kuchitika-Watero Chaponda

Kulowa m’boma kwa Chipani cha MCP ndi ngozi yomwe simayenera kuchitika-Watero Chaponda

Mtsogoleli wa zipani zotsutsa mnyumba ya malamulo Dr. George Chaponda wati kulowa m’boma kwa chipani cha MCP ndi ngozi yomwe simayenera kuchitika.

Chaponda wati chipani cha Democratic Progressive (DPP) chidzapambana chisankho cha pa 16 September chaka chino.

Dr. Chaponda anena izi m’mawa uno pomwe aphungu a nyumba yamalamulo akukumana kotsiliza chiwasankhireni pachisankho cha 2019.

Iwo akuti a Peter Mutharika ndi omwe angathane ndi mavuto omwe dziko lino likukumana nawo.

Wolemba: Esther Nyirongo, Lilongwe.

liwulanulachikondi

RELATED ARTICLES

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

- Advertisment -

Most Popular