spot_img
spot_img
19.2 C
New York
Sunday, October 6, 2024
spot_img
spot_img

Amayi ku Chiradzulu akukana kugwiritsa ntchito makondomu

….Ati amaononga chisangalalo ku chipinda pogagadana!

Zadziwika kuti amayi ambiri m’boma la Chiradzulu sakonda kugwiritsa ntchito makondomu achizimayi zomwe zikupangitsa kuti makondomu-wa adziwonongeka.

Izi zadziwika pa mkumano waatsogoleri osiyanasiyana omwe amaunika m’mene akugwilira ntchito pa nkhani zokhudza HIV m’boma la Chiradzulu.

Glory Shaba, yemwe ndi mkulu oyang’anira ndondomeko yogawa makondomu m’bomali, wati pa Chipatala cha m’bomali makondomu amayi akumapanga “expire” asanagwiritsidwe ntchito.

Malingana ndi a Shaba, izi ndi kammba koti amayi ambiri sakumapita ku chipatalachi kuti akatenge makondomuwo.

M’mawu ake Shabam wati vutoli lakula chifukwa choti adindo sakutengapo gawo kwenikweni kufalitsa ubwino ogwilitsa ntchito makondomuwa.

Related Articles

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

- Advertisement -

Latest Articles